Dataset Viewer
Auto-converted to Parquet
similarity
float32
1.05
1.25
English
stringlengths
1
500
Chichewa
stringlengths
3
500
1.249614
What is it that these people testify against You?"
Kodi umboni umenewu ndi otani umene anthu awa akupereka kukutsutsa Iwe?"
1.24933
All three made these changes because they wanted to be like Christ.
Anthu atatu onsewa anasintha chonchi chifukwa choti ankafuna kutsanzira Khristu.
1.248731
And he and his hosts were arrogant in the land, without right, and they thought that they would never return to Us
"Ndipo iye pamodzi ndi makamu ake ankhondo adadzitukumula pa dziko popanda chilungamo ndipo ankaganiza kuti iwo sadzabwelere kwa Ife.
1.248266
what ways they are deluded away from the truth!
njira yanji akuchotsedwa ku (choonadi)!
1.248011
And fear the Fire, which is prepared for the disbelievers.)
"Ndipo opani Moto umene wakonzedwa kwa (anthu) osakhulupirira.
1.24708
Ask them about the town that was present by the sea, when they overstepped in Sabbath.
"Tawafunsani nkhani ya mudzi umene udali m'mphepete mwa nyanja; (anthu am'mudziwo) pamene adali kuswa (lamulo la) tsiku la Sabata (lomwe adauzidwa kuti pa tsikuli asamachite usodzi wa nsomba, koma m'malo mwake azichita mapemphero okha).
1.246966
"It is He Who gives life and causes death - your Lord and the Lord of your forefathers."
Amapereka moyo ndikupereka imfa, Mbuye wanu ndi Mbuye wa makolo anu oyamba.
1.246914
Thus We caused Joseph to be established in a position of authority in the land.
"Ndipo motero tidampatsa ulemelero Yûsuf m'dziko (la Iguputo); amakhala m'menemo paliponse pamene wafuna.
1.246814
Man says, "When I am dead, shall I be brought forth alive?"
"Ndipo munthu (wokanira) amanena: "Kodi ndikadzafa nzoonadi kuti Ndidzatulutsidwa (m'manda) nkukhala wamoyo?"
1.246633
He walked with Me in peace and uprightness, and turned away many from iniquity.
Iye anayenda nane mwamtendere ndi molungama mtima, ndipo anabweza anthu ambiri mʼnjira zawo zauchimo.
1.246354
Or, "who has first given to him, so that it must be repaid to him?"
Kapenanso, 'Ndani anayamba kumupatsa kanthu, kuti amubwezere?'
1.24617
That is what pushed them to accomplish what they did."
N'zimene zinawasonkhezera kukwaniritsa zimene anachita."
1.245136
Was the language of the Qur'an Arabic?
Kodi Qur'an sinadzudzule ma Arabu achikunja chifukwa
1.244692
Although his presence as King of God's Kingdom is invisible, it is obvious from the fulfillment of prophecies.
Ngakhale kuti kukhalapo kwake monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu n'kosaoneka, umboni wake ukuoneka chifukwa cha kukwaniritsidwa kwa maulosi.
1.244652
And the Aad. they were destroyed by a fierce roaring wind.
Ndipo A'adi adaonongedwa ndi chimphepo
1.244138
But the recompense of your Lord is best, and He is the best of those who provide sustenance (72)
Koma malipiro a Mbuye wako ndiwo abwino; ndipo Iye ndi Wopereka Wabwino kuposa opereka.
1.24336
Then he called upon his Lord, "These are a guilty people."
Ndipo iye adaitana Mbuye wake kuti: "Awa ndithu ndi anthu oipa."
1.242762
They are the ones who bought the life of this world for the Hereafter; so their punishment shall not be lightened, nor will they be helped. (86)
" Iwowo ndi amene asinthanitsa moyo wa dziko lapansi ndi moyo ulinkudza choncho sadzawachepetsera chilango, ndiponso sadzapulumutsidwa.
1.242308
(23) Then you will go on your way in safety, and your foot will not stumble.
Ukatero udzayenda panjira yako popanda chokuopseza, ndipo ngakhale phazi lako silidzapunthwa ndi chilichonse."
1.241669
"God is my Lord and your Lord, so serve Him: that is a straight path."
""Ndithu Allah ndiye Mbuye wanga ndi Mbuye wanunso; choncho mupembedzeni; imeneyi ndiyo njira yolunjika."
1.241305
And the fifth time: that Allah's curse be upon him, if he is a liar.
"Ndipo kachisanu (alumbire) kuti matembelero a Allah akhale pa iye ngati (iye) ali m'modzi mwa onama.
1.24095
then every soul will know what it has brought about."
(Zikadzachitika zimenezi) mzimu Uliwonse udzadziwa zimene Wabweretsa (zabwino ndi zoipa).
1.240341
To escape from the lake of fire, there is no other way but to have our names written in the Book of Life.
Kuti tithawe kuchoka mnyanja yamoto, kulibe njira ina iliyonse koma kuti maina athu alembedwe mu Buku la Moyo.
1.240003
They leave their wealth to others.
ndipo amasiyira chuma chawo anthu ena.
1.239921
"And we have left a clear sign of it for people who possess intellects."
"Ndipo ndithu tidasiya chizindikiro mmenemo choonekera kwa anthu anzeru.
1.239803
Send forth your Spirit and they shall be created.
Atumize Mzimu Wanu, ndipo iwo adzakhala analenga.
1.239669
But worship Allah alone and be among the grateful" [Qur'an, 39:66].
"Koma pembedza Allah yekha, ndipo khala mwa othokoza.
1.239245
Don't they see how Allah originates the creation, and then repeats it?
"Kodi saona momwe Allah ayambitsira zolengedwa, kenako nkuzibwerezanso?
1.239112
"And for he who feared the majesty of his Lord, there will be two gardens."
"Koma amene waopa kuti adzaimitsidwa kwa Mbuye wake (pa nthawi ya chiweruziro), adzalandira minda iwiri (yaikulu yamtendere).
1.23881
Still my lord the king is as the angel of God, so do what seems best to you.
Koma inu mbuyanga mfumu muli ngati mngelo+ wa Mulungu woona, motero chitani zimene zili zabwino kwa inu.
1.238683
If you ask them: "Who created them?"
"Ndipo ngati utawafunsa: "Ndani adawalenga?"
1.238638
"Surely Allah loves those who fight in His way in ranks as if they were a firm and compact wall."
"Ndithu Allah amakonda amene akumenya nkhondo pa njira Yake (yofalitsa chipembedzo Chake), ali pa mzere (umodzi) uku ali monga chomanga, chomangika mwamphamvu.
1.238579
And that is how We make clear the verses (provide details) so, that maybe they will return.
"M'menemo ndi momwe tikulongosolera mokwanira zivumbulutso kuti mwina iwo angabwelere (kwa Allah).
1.237748
I gathered together all their inhabitants and restored to them their dwellings."
(Komanso) ndinasonkhanitsa anthu onse (amene ankakhala m'mizindayo) ndipo ndinawalamula kuti abwerere kumizinda yawo."
1.237373
Then they will live in their own land, which I gave to My servant Ja'acov.
Ndipo iwo adzakhala ndi moyo m'dziko lawo, limene ndinapatsa mtumiki wanga Yakobo.
1.237315
but those who seek to go beyond that are transgressors --
Koma amene angafune (zina) Kusiya zimenezi iwowo ndiwo Olumpha malire.
1.237193
In this is a sign for every obedient servant.
Ndithu m'zimenezo muli malingaliro kwa kapolo aliyense wotembenukira (kwa Allah).
1.237172
I fear for you the punishment of a great Day."
""Ndithu ine ndikukuoperani chilango cha tsiku lalikulu."
1.236793
He will take them into gardens with rivers flowing beneath them, where they will live forever.
Ndipo adzawalowetsa m'minda yomwe pansi pake pakuyenda mitsinje; adzakhala m'menemo muyaya.
1.236745
then every soul will know what it has brought about."
" (Zikadzachitika zimenezi) mzimu uliwonse udzadziwa zimene wabweretsa (zabwino ndi zoipa).
1.23629
Whomsoever You cause to enter Hell, him You have surely disgraced, and for the wrongdoers there shall be no helpers."
Ndithudi, yemwe mudzamulowetse ku Moto ndiye kuti mwamuyalutsa, ndipo sipadzakhala athandizi kwa ochita zoipa."
1.236036
The two angels came to Sodom in the evening, and Lot was sitting in the gate of Sodom.
"Ndipo angelo awiriwa anadza ku Sodomu madzulo, pamene Loti adakhala pachipata cha Sodomu.
1.235174
Moreover, we are assured: "It will turn out well with those fearing the true God."
Komanso tikulimbikitsidwa ndi mawu akuti: 'Omwe aopa Mulungu adzapeza bwino.'
1.234758
To whomsoever of you wills to walk straight.
"Kwa yemwe mwa inu akufuna kuyenda mu njira yoongoka.
1.234457
(18) And so we awaked them from their sleep, that they might ask questions of one another.
"Ndipo momwemonso tidawautsa kuti afunsane pakati pawo (zanthawi imene akhala ali chigonere).
1.234444
So that a man shall say, no doubt,
Ndipo munthu adati kwa ena,
1.233764
When you come out, you will be old and alone."
Ukadzatuluka udzakhala wokalamba komanso wekhawekha."
1.233684
Allah has revealed the holy Qur'an in the month of Ramadan.
Qur'an inabvumbulutsidwa Mmwezi wa Ramadhan, choncho Allah anaupanga mwezi wa Ramadhan kukhala wabwino kuposa myezi yonse.
1.233576
We sent down upon them a violent sandstorm (which destroyed them all) except for the family of Lot, whom We saved in the early morning by Our favor.
"Ndithu Ife tidawatumizira chimphepo champhamvu choulutsa miyala (ndi kuwagenda), kupatula akubanja la Luti; tidawapulumutsa (ku chilangocho) m'bandakucha,
1.233007
For the days of my people will be like the days of a tree, and the work of their hands my chosen ones will enjoy to the full."
Thangwe nsiku za wanthu wangu, zin'dzakhala ninga nsiku za muti, ndipo omwe ndawasankhulawo, wan'dzapfatsa na mabasa yakuphatidwa na manja yawo.'
1.232809
Fear God, and know that God is severe in retribution.
Ndipo opani Allah, dziwani kuti Allah Ngwaukali polanga.
1.232695
I am but a Warner and the giver of good news to the people who believe."
Ine sindili chilichonse koma mchenjezi ndi wouza anthu okhulupirira nkhani zabwino."
1.232479
Douglas, our blog has been the same since 1999.
Douglas, blog yathu yakhala chimodzimodzi kuyambira 1999.
1.232425
From heaven or from men."
Kumwamba kapena kwa anthu?"
1.232409
Hell is a place to be feared.
Ngati helo alidi malo ozunzirako anthu, m'pake kuopa.
1.232271
"Then it will be said to those who were unjust, 'Taste the eternal punishment.
"Kenako kudzanenedwa kwa amene adachita zoipa: "Lawani chilango chamuyaya!
1.231721
when Our clear revelations are recited to them, is to say, 'Bring back our forefathers if what you say is true.'
"Ndipo Ayah Zathu zikawerengcdwa kwa iwo zolongosola chilichonse momveka, alibe mtsutso wina koma kunena kuti: "Tibweretsereni makolo Athu (aukitseni akhale ndi moyo) ngati inu muli owona!"
1.231489
"Except for Your chosen servants among them."
""Kupatula akapolo Anu omwe ali osankhidwa (oyeretsedwa) mwa iwo.
1.231091
"Say: 'O' People of the Book Why do you disbelieve in the Signs of Allah, while Allah is Witness to what you do?"
"Nena: "E inu amene mudapatsidwa buku! chifukwa chiyani mukuzikana zizindikiro za Allah pomwe Allah ndi Mboni wa zonse zimene mukuchita?"
1.230943
The sky is still clear, which is a great sign.
Komabe, umboni wosatulutsa mawu wa zinthu zakumwamba ndi wamphamvu kwambiri.
1.230845
"How then could we steal silver or gold from your lord's house.
Kotero kodi izo kutsatira kuti ife kuba, ku nyumba ya mbuye wanu, golide kapena siliva?
1.230769
How many cities We have destroyed, greater in strength than your city which has driven you out, and there was no one to help them.
"Ndi ambiri mwa eni mizinda (yakale) omwe adali amphamvu kuposa eni mzinda wakowu umene akutulutsamo (eni ake,) tidawaononga (ndi zilango zosiyanasiyana) koma padalibe wowateteza (kwa Ife).
1.230078
We have been taught the speech of the birds, and have been given all kinds of things.
Ndithu taphunzitsidwa (mpaka tikudziwa) chiyankhulo cha mbalame, ndiponso tapatsidwa chilichonse; ndithu umenewu ndiubwino wopenyeka.
1.229597
Joseph asks, "Why are your faces sad today?"
Yosefe atawaona, anazindikira kuti akuda nkhawa ndi zinazake ndipo anawafunsa kuti: "N'chifukwa chiyani nkhope zanu zili zachisoni lero?"
1.229514
Your Promise is true, and You are the Most Just of the judges.'
Ndipo ndithu lonjezo lanu ndiloona, ndipo Inu Ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse."
1.229388
And We saved him and his family from the Great Affliction.
"Ndipo tidampulumutsa iye ndi anthu ake ku vuto lalikulu.
1.229292
If you find yourself in either situation, consider the example of Moses.
Ngati ndinu wachinyamata ndipo mwakumana ndi zimenezi, muyenera kuganizira za Mose.
1.229268
Did they not see that it could not speak to them, nor guide them in any way?
Kodi sakuona kuti ilo (fano lawolo) silikuwalankhula ndiponso silikuwaongolera njira (yabwino?)
1.229266
"Indeed We see the turning of your face to heaven.
"Ndithudi, taona kutembenukatembenuka kwa nkhope yako (kuyang'ana) kumwamba.
1.229064
The Lord is near."
Ambuye ali pafupi."
1.229047
The god struck him with an illness.
Choncho Mulungu anamulanga ndi matenda oopsa akhate.
1.228912
Your Promise is true, and You are the Most Just of the judges.'
Ndipo ndithu, lonjezo lanu ndiloona, ndipo inu ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse."
1.22869
We provide help to all; to these (seekers of this world) and to those (seekers of the Hereafter), by the Bestowal of your Lord; and there is no stoppage on the Bestowal of your Lord,'
"Onse awa, (abwino ndi oipa), timawapatsa awa ndi awa mwazopatsa za Mbuye wako; ndipo zopatsa za Mbuye wako sizotsekerezedwa (kuti zisamfike kapolo Wake).
1.228387
Let him bring us a sign, just as the ancient ones were sent asMessengers'
Chonchotu, atibweretsere chizizwa monga mmene adatumiziridwa (aneneri) oyamba."
1.228307
Verily, We sent against them a violent storm of stones (which destroyed them all), except the family of Lout (Lot), whom We saved in last hour of the night,
"Ndithu Ife tidawatumizira chimphepo champhamvu choulutsa miyala (ndi kuwagenda), kupatula akubanja la Luti; tidawapulumutsa (ku chilangocho) m'bandakucha,
1.228207
How do you see the punishment
Ameneyu ndiye mwamuwona kuti ndiye wofunika punishment?
1.228024
And he said, "Behold, the fire and the wood, but
Taonani,"Iye anati, "Moto ndi nkhuni.
1.227569
"That is because Allah is the Truth, and that which they call upon besides Him; that is the falsehood..."1
"Zimenezo nchifukwa chakuti Allah ndi Wowona (alipo;) ndipo zimene akuzipembedza kusiya Iye, nzachabe.
1.22756
The promise of our Lord is done." ‹
Ndithu lonjezo la Mbuye wathu ndi lokwaniritsidwa!"
1.227452
Or the feeding on a day of hunger.
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa masiku a njala.
1.227209
Will they be able to help you?"
Kodi angathe kukuthandizani kapena kudzithandiza okha?"
1.227205
Your Lord said, "That is easy for Me and I created you before when you were nothing."
Mbuye wako wanena (kuti): 'Izi nzofewa kwa Ine; ndithu ndidakulenga kale pomwe iwe sudali kanthu."
1.227189
Speak to him in a soft manner; maybe he will take admonition or fear.
"Kamuuzeni mawu ofewa mwina akalingalira (uthengawo) kapena akaopa.
1.227084
"Embark therein; in the Name of God will be its course and its anchorage.
"Ndipo (Nuh) adati: "Kwerani m'menemo mwadzina la Allah mkuyenda kwake ndi mkukocheza kwake.
1.227064
Or the feeding on a day of hunger.
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa Masiku a njala
1.226681
As you read it, remember that it is God's message to you as an individual.
Pamene muwerenga, kumbukirani ndi uthenga wa Mulungu kwa inu ngati munthu.
1.226598
fear Him Who has created you and those who have gone before you."
""Ndipo muopeni amene adalenga inu ndiponso zolengedwa zoyamba (zimene zidanka kale)."
1.226476
"And we divided them into twelve decedent tribes."
"Ndipo tidawagawa iwo m'mafuko khumi ndi awiri (osiyanasiyana) monga mitundu ikuluikulu.
1.226075
1 A day with your Lord is equivalent to a thousand years in the way you count.
Ndipo ndithu tsiku limodzi kwa Mbuye wako lili ngati zaka chikwi chimodzi mukawerengedwe kanu.
1.226
and gives birth to the other.
mwanayo) adzamuyamwitsira (mkazi) wina,
1.225904
And from those, We have created, there is a group of people who guide others with the truth.
"Ndipo mwa amene tidawalenga, alipo anthu oongolera (anzawo) ku choonadi.
1.225893
[21.111] "I know not but that it may be a trial for you, and a grant of (worldly) livelihood (to you) for a time."
""Ndipo sindikudziwa, mwina kuchedwetsa chilango chanu ndi mayeso akukuyesani ndikukusangalatsani ndi zokoma (za m'dziko) mpaka Idzakwane nthawi yoikidwayo."
1.225869
Or they may fear that they will find it difficult to live up to God's requirements after baptism.
Kapena angachite mantha kuti zidzawavuta kuchita zimene Mulungu amafuna akadzabatizidwa.
1.225816
"Why do you sit by yourself, and all the people stand before you from morning until evening?"
N'chifukwa chiyani wangokhala wekha kupereka ziweruzo ndipo anthu onse ali chiimire pamaso pako kuyambira m'mawa mpaka madzulo?"
1.225771
When she expressed this concern, Jesus plainly said to her: "You worship what you do not know."
Atamuuza vutoli, Yesu anamuuza momveka bwino kuti: "Inu mumalambira chimene simuchidziwa."
1.225752
shall not be accepted from them, and they shall have a painful punishment.
Ndiponso sadzawayeretsa (kumachimo awo); ndipo iwo adzapeza chilango chopweteka.
1.225608
it is a sound of a single-coil
monga mawu omveka, pamene khoma limodzi limaphimbidwa;
1.225388
And, indeed, I think he is a liar!"
Ndithu ine ndikumganizira kuti ndi mmodzi wa abodza."
1.225353
God answered the prayers of Solomon.
Mwachitsanzo, Solomo anachonderera Mulungu kuti aziyankha mapembedzero a olambira Ake.
1.225239
in God I have put my trust, I shall not be afraid.
mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha.
End of preview. Expand in Data Studio
README.md exists but content is empty.
Downloads last month
66

Collection including michsethowusu/english-chichewa_sentence-pairs