African-English Parallel Sentences
Collection
Collection of sentence pairs or parallel corpus of African Languages and English for machine translation.
•
46 items
•
Updated
similarity
float32 1.05
1.25
⌀ | English
stringlengths 1
500
| Chichewa
stringlengths 3
500
|
---|---|---|
1.249614 | What is it that these people testify against You?" | Kodi umboni umenewu ndi otani umene anthu awa akupereka kukutsutsa Iwe?" |
1.24933 | All three made these changes because they wanted to be like Christ. | Anthu atatu onsewa anasintha chonchi chifukwa choti ankafuna kutsanzira Khristu. |
1.248731 | And he and his hosts were arrogant in the land, without right, and they thought that they would never return to Us | "Ndipo iye pamodzi ndi makamu ake ankhondo adadzitukumula pa dziko popanda chilungamo ndipo ankaganiza kuti iwo sadzabwelere kwa Ife. |
1.248266 | what ways they are deluded away from the truth! | njira yanji akuchotsedwa ku (choonadi)! |
1.248011 | And fear the Fire, which is prepared for the disbelievers.) | "Ndipo opani Moto umene wakonzedwa kwa (anthu) osakhulupirira. |
1.24708 | Ask them about the town that was present by the sea, when they overstepped in Sabbath. | "Tawafunsani nkhani ya mudzi umene udali m'mphepete mwa nyanja; (anthu am'mudziwo) pamene adali kuswa (lamulo la) tsiku la Sabata (lomwe adauzidwa kuti pa tsikuli asamachite usodzi wa nsomba, koma m'malo mwake azichita mapemphero okha). |
1.246966 | "It is He Who gives life and causes death - your Lord and the Lord of your forefathers." | Amapereka moyo ndikupereka imfa, Mbuye wanu ndi Mbuye wa makolo anu oyamba. |
1.246914 | Thus We caused Joseph to be established in a position of authority in the land. | "Ndipo motero tidampatsa ulemelero Yûsuf m'dziko (la Iguputo); amakhala m'menemo paliponse pamene wafuna. |
1.246814 | Man says, "When I am dead, shall I be brought forth alive?" | "Ndipo munthu (wokanira) amanena: "Kodi ndikadzafa nzoonadi kuti Ndidzatulutsidwa (m'manda) nkukhala wamoyo?" |
1.246633 | He walked with Me in peace and uprightness, and turned away many from iniquity. | Iye anayenda nane mwamtendere ndi molungama mtima, ndipo anabweza anthu ambiri mʼnjira zawo zauchimo. |
1.246354 | Or, "who has first given to him, so that it must be repaid to him?" | Kapenanso, 'Ndani anayamba kumupatsa kanthu, kuti amubwezere?' |
1.24617 | That is what pushed them to accomplish what they did." | N'zimene zinawasonkhezera kukwaniritsa zimene anachita." |
1.245136 | Was the language of the Qur'an Arabic? | Kodi Qur'an sinadzudzule ma Arabu achikunja chifukwa |
1.244692 | Although his presence as King of God's Kingdom is invisible, it is obvious from the fulfillment of prophecies. | Ngakhale kuti kukhalapo kwake monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu n'kosaoneka, umboni wake ukuoneka chifukwa cha kukwaniritsidwa kwa maulosi. |
1.244652 | And the Aad. they were destroyed by a fierce roaring wind. | Ndipo A'adi adaonongedwa ndi chimphepo |
1.244138 | But the recompense of your Lord is best, and He is the best of those who provide sustenance (72) | Koma malipiro a Mbuye wako ndiwo abwino; ndipo Iye ndi Wopereka Wabwino kuposa opereka. |
1.24336 | Then he called upon his Lord, "These are a guilty people." | Ndipo iye adaitana Mbuye wake kuti: "Awa ndithu ndi anthu oipa." |
1.242762 | They are the ones who bought the life of this world for the Hereafter; so their punishment shall not be lightened, nor will they be helped. (86) | " Iwowo ndi amene asinthanitsa moyo wa dziko lapansi ndi moyo ulinkudza choncho sadzawachepetsera chilango, ndiponso sadzapulumutsidwa. |
1.242308 | (23) Then you will go on your way in safety, and your foot will not stumble. | Ukatero udzayenda panjira yako popanda chokuopseza, ndipo ngakhale phazi lako silidzapunthwa ndi chilichonse." |
1.241669 | "God is my Lord and your Lord, so serve Him: that is a straight path." | ""Ndithu Allah ndiye Mbuye wanga ndi Mbuye wanunso; choncho mupembedzeni; imeneyi ndiyo njira yolunjika." |
1.241305 | And the fifth time: that Allah's curse be upon him, if he is a liar. | "Ndipo kachisanu (alumbire) kuti matembelero a Allah akhale pa iye ngati (iye) ali m'modzi mwa onama. |
1.24095 | then every soul will know what it has brought about." | (Zikadzachitika zimenezi) mzimu Uliwonse udzadziwa zimene Wabweretsa (zabwino ndi zoipa). |
1.240341 | To escape from the lake of fire, there is no other way but to have our names written in the Book of Life. | Kuti tithawe kuchoka mnyanja yamoto, kulibe njira ina iliyonse koma kuti maina athu alembedwe mu Buku la Moyo. |
1.240003 | They leave their wealth to others. | ndipo amasiyira chuma chawo anthu ena. |
1.239921 | "And we have left a clear sign of it for people who possess intellects." | "Ndipo ndithu tidasiya chizindikiro mmenemo choonekera kwa anthu anzeru. |
1.239803 | Send forth your Spirit and they shall be created. | Atumize Mzimu Wanu, ndipo iwo adzakhala analenga. |
1.239669 | But worship Allah alone and be among the grateful" [Qur'an, 39:66]. | "Koma pembedza Allah yekha, ndipo khala mwa othokoza. |
1.239245 | Don't they see how Allah originates the creation, and then repeats it? | "Kodi saona momwe Allah ayambitsira zolengedwa, kenako nkuzibwerezanso? |
1.239112 | "And for he who feared the majesty of his Lord, there will be two gardens." | "Koma amene waopa kuti adzaimitsidwa kwa Mbuye wake (pa nthawi ya chiweruziro), adzalandira minda iwiri (yaikulu yamtendere). |
1.23881 | Still my lord the king is as the angel of God, so do what seems best to you. | Koma inu mbuyanga mfumu muli ngati mngelo+ wa Mulungu woona, motero chitani zimene zili zabwino kwa inu. |
1.238683 | If you ask them: "Who created them?" | "Ndipo ngati utawafunsa: "Ndani adawalenga?" |
1.238638 | "Surely Allah loves those who fight in His way in ranks as if they were a firm and compact wall." | "Ndithu Allah amakonda amene akumenya nkhondo pa njira Yake (yofalitsa chipembedzo Chake), ali pa mzere (umodzi) uku ali monga chomanga, chomangika mwamphamvu. |
1.238579 | And that is how We make clear the verses (provide details) so, that maybe they will return. | "M'menemo ndi momwe tikulongosolera mokwanira zivumbulutso kuti mwina iwo angabwelere (kwa Allah). |
1.237748 | I gathered together all their inhabitants and restored to them their dwellings." | (Komanso) ndinasonkhanitsa anthu onse (amene ankakhala m'mizindayo) ndipo ndinawalamula kuti abwerere kumizinda yawo." |
1.237373 | Then they will live in their own land, which I gave to My servant Ja'acov. | Ndipo iwo adzakhala ndi moyo m'dziko lawo, limene ndinapatsa mtumiki wanga Yakobo. |
1.237315 | but those who seek to go beyond that are transgressors -- | Koma amene angafune (zina) Kusiya zimenezi iwowo ndiwo Olumpha malire. |
1.237193 | In this is a sign for every obedient servant. | Ndithu m'zimenezo muli malingaliro kwa kapolo aliyense wotembenukira (kwa Allah). |
1.237172 | I fear for you the punishment of a great Day." | ""Ndithu ine ndikukuoperani chilango cha tsiku lalikulu." |
1.236793 | He will take them into gardens with rivers flowing beneath them, where they will live forever. | Ndipo adzawalowetsa m'minda yomwe pansi pake pakuyenda mitsinje; adzakhala m'menemo muyaya. |
1.236745 | then every soul will know what it has brought about." | " (Zikadzachitika zimenezi) mzimu uliwonse udzadziwa zimene wabweretsa (zabwino ndi zoipa). |
1.23629 | Whomsoever You cause to enter Hell, him You have surely disgraced, and for the wrongdoers there shall be no helpers." | Ndithudi, yemwe mudzamulowetse ku Moto ndiye kuti mwamuyalutsa, ndipo sipadzakhala athandizi kwa ochita zoipa." |
1.236036 | The two angels came to Sodom in the evening, and Lot was sitting in the gate of Sodom. | "Ndipo angelo awiriwa anadza ku Sodomu madzulo, pamene Loti adakhala pachipata cha Sodomu. |
1.235174 | Moreover, we are assured: "It will turn out well with those fearing the true God." | Komanso tikulimbikitsidwa ndi mawu akuti: 'Omwe aopa Mulungu adzapeza bwino.' |
1.234758 | To whomsoever of you wills to walk straight. | "Kwa yemwe mwa inu akufuna kuyenda mu njira yoongoka. |
1.234457 | (18) And so we awaked them from their sleep, that they might ask questions of one another. | "Ndipo momwemonso tidawautsa kuti afunsane pakati pawo (zanthawi imene akhala ali chigonere). |
1.234444 | So that a man shall say, no doubt, | Ndipo munthu adati kwa ena, |
1.233764 | When you come out, you will be old and alone." | Ukadzatuluka udzakhala wokalamba komanso wekhawekha." |
1.233684 | Allah has revealed the holy Qur'an in the month of Ramadan. | Qur'an inabvumbulutsidwa Mmwezi wa Ramadhan, choncho Allah anaupanga mwezi wa Ramadhan kukhala wabwino kuposa myezi yonse. |
1.233576 | We sent down upon them a violent sandstorm (which destroyed them all) except for the family of Lot, whom We saved in the early morning by Our favor. | "Ndithu Ife tidawatumizira chimphepo champhamvu choulutsa miyala (ndi kuwagenda), kupatula akubanja la Luti; tidawapulumutsa (ku chilangocho) m'bandakucha, |
1.233007 | For the days of my people will be like the days of a tree, and the work of their hands my chosen ones will enjoy to the full." | Thangwe nsiku za wanthu wangu, zin'dzakhala ninga nsiku za muti, ndipo omwe ndawasankhulawo, wan'dzapfatsa na mabasa yakuphatidwa na manja yawo.' |
1.232809 | Fear God, and know that God is severe in retribution. | Ndipo opani Allah, dziwani kuti Allah Ngwaukali polanga. |
1.232695 | I am but a Warner and the giver of good news to the people who believe." | Ine sindili chilichonse koma mchenjezi ndi wouza anthu okhulupirira nkhani zabwino." |
1.232479 | Douglas, our blog has been the same since 1999. | Douglas, blog yathu yakhala chimodzimodzi kuyambira 1999. |
1.232425 | From heaven or from men." | Kumwamba kapena kwa anthu?" |
1.232409 | Hell is a place to be feared. | Ngati helo alidi malo ozunzirako anthu, m'pake kuopa. |
1.232271 | "Then it will be said to those who were unjust, 'Taste the eternal punishment. | "Kenako kudzanenedwa kwa amene adachita zoipa: "Lawani chilango chamuyaya! |
1.231721 | when Our clear revelations are recited to them, is to say, 'Bring back our forefathers if what you say is true.' | "Ndipo Ayah Zathu zikawerengcdwa kwa iwo zolongosola chilichonse momveka, alibe mtsutso wina koma kunena kuti: "Tibweretsereni makolo Athu (aukitseni akhale ndi moyo) ngati inu muli owona!" |
1.231489 | "Except for Your chosen servants among them." | ""Kupatula akapolo Anu omwe ali osankhidwa (oyeretsedwa) mwa iwo. |
1.231091 | "Say: 'O' People of the Book Why do you disbelieve in the Signs of Allah, while Allah is Witness to what you do?" | "Nena: "E inu amene mudapatsidwa buku! chifukwa chiyani mukuzikana zizindikiro za Allah pomwe Allah ndi Mboni wa zonse zimene mukuchita?" |
1.230943 | The sky is still clear, which is a great sign. | Komabe, umboni wosatulutsa mawu wa zinthu zakumwamba ndi wamphamvu kwambiri. |
1.230845 | "How then could we steal silver or gold from your lord's house. | Kotero kodi izo kutsatira kuti ife kuba, ku nyumba ya mbuye wanu, golide kapena siliva? |
1.230769 | How many cities We have destroyed, greater in strength than your city which has driven you out, and there was no one to help them. | "Ndi ambiri mwa eni mizinda (yakale) omwe adali amphamvu kuposa eni mzinda wakowu umene akutulutsamo (eni ake,) tidawaononga (ndi zilango zosiyanasiyana) koma padalibe wowateteza (kwa Ife). |
1.230078 | We have been taught the speech of the birds, and have been given all kinds of things. | Ndithu taphunzitsidwa (mpaka tikudziwa) chiyankhulo cha mbalame, ndiponso tapatsidwa chilichonse; ndithu umenewu ndiubwino wopenyeka. |
1.229597 | Joseph asks, "Why are your faces sad today?" | Yosefe atawaona, anazindikira kuti akuda nkhawa ndi zinazake ndipo anawafunsa kuti: "N'chifukwa chiyani nkhope zanu zili zachisoni lero?" |
1.229514 | Your Promise is true, and You are the Most Just of the judges.' | Ndipo ndithu lonjezo lanu ndiloona, ndipo Inu Ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse." |
1.229388 | And We saved him and his family from the Great Affliction. | "Ndipo tidampulumutsa iye ndi anthu ake ku vuto lalikulu. |
1.229292 | If you find yourself in either situation, consider the example of Moses. | Ngati ndinu wachinyamata ndipo mwakumana ndi zimenezi, muyenera kuganizira za Mose. |
1.229268 | Did they not see that it could not speak to them, nor guide them in any way? | Kodi sakuona kuti ilo (fano lawolo) silikuwalankhula ndiponso silikuwaongolera njira (yabwino?) |
1.229266 | "Indeed We see the turning of your face to heaven. | "Ndithudi, taona kutembenukatembenuka kwa nkhope yako (kuyang'ana) kumwamba. |
1.229064 | The Lord is near." | Ambuye ali pafupi." |
1.229047 | The god struck him with an illness. | Choncho Mulungu anamulanga ndi matenda oopsa akhate. |
1.228912 | Your Promise is true, and You are the Most Just of the judges.' | Ndipo ndithu, lonjezo lanu ndiloona, ndipo inu ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse." |
1.22869 | We provide help to all; to these (seekers of this world) and to those (seekers of the Hereafter), by the Bestowal of your Lord; and there is no stoppage on the Bestowal of your Lord,' | "Onse awa, (abwino ndi oipa), timawapatsa awa ndi awa mwazopatsa za Mbuye wako; ndipo zopatsa za Mbuye wako sizotsekerezedwa (kuti zisamfike kapolo Wake). |
1.228387 | Let him bring us a sign, just as the ancient ones were sent asMessengers' | Chonchotu, atibweretsere chizizwa monga mmene adatumiziridwa (aneneri) oyamba." |
1.228307 | Verily, We sent against them a violent storm of stones (which destroyed them all), except the family of Lout (Lot), whom We saved in last hour of the night, | "Ndithu Ife tidawatumizira chimphepo champhamvu choulutsa miyala (ndi kuwagenda), kupatula akubanja la Luti; tidawapulumutsa (ku chilangocho) m'bandakucha, |
1.228207 | How do you see the punishment | Ameneyu ndiye mwamuwona kuti ndiye wofunika punishment? |
1.228024 | And he said, "Behold, the fire and the wood, but | Taonani,"Iye anati, "Moto ndi nkhuni. |
1.227569 | "That is because Allah is the Truth, and that which they call upon besides Him; that is the falsehood..."1 | "Zimenezo nchifukwa chakuti Allah ndi Wowona (alipo;) ndipo zimene akuzipembedza kusiya Iye, nzachabe. |
1.22756 | The promise of our Lord is done." ‹ | Ndithu lonjezo la Mbuye wathu ndi lokwaniritsidwa!" |
1.227452 | Or the feeding on a day of hunger. | Kapena kuwadyetsa (osowa) pa masiku a njala. |
1.227209 | Will they be able to help you?" | Kodi angathe kukuthandizani kapena kudzithandiza okha?" |
1.227205 | Your Lord said, "That is easy for Me and I created you before when you were nothing." | Mbuye wako wanena (kuti): 'Izi nzofewa kwa Ine; ndithu ndidakulenga kale pomwe iwe sudali kanthu." |
1.227189 | Speak to him in a soft manner; maybe he will take admonition or fear. | "Kamuuzeni mawu ofewa mwina akalingalira (uthengawo) kapena akaopa. |
1.227084 | "Embark therein; in the Name of God will be its course and its anchorage. | "Ndipo (Nuh) adati: "Kwerani m'menemo mwadzina la Allah mkuyenda kwake ndi mkukocheza kwake. |
1.227064 | Or the feeding on a day of hunger. | Kapena kuwadyetsa (osowa) pa Masiku a njala |
1.226681 | As you read it, remember that it is God's message to you as an individual. | Pamene muwerenga, kumbukirani ndi uthenga wa Mulungu kwa inu ngati munthu. |
1.226598 | fear Him Who has created you and those who have gone before you." | ""Ndipo muopeni amene adalenga inu ndiponso zolengedwa zoyamba (zimene zidanka kale)." |
1.226476 | "And we divided them into twelve decedent tribes." | "Ndipo tidawagawa iwo m'mafuko khumi ndi awiri (osiyanasiyana) monga mitundu ikuluikulu. |
1.226075 | 1 A day with your Lord is equivalent to a thousand years in the way you count. | Ndipo ndithu tsiku limodzi kwa Mbuye wako lili ngati zaka chikwi chimodzi mukawerengedwe kanu. |
1.226 | and gives birth to the other. | mwanayo) adzamuyamwitsira (mkazi) wina, |
1.225904 | And from those, We have created, there is a group of people who guide others with the truth. | "Ndipo mwa amene tidawalenga, alipo anthu oongolera (anzawo) ku choonadi. |
1.225893 | [21.111] "I know not but that it may be a trial for you, and a grant of (worldly) livelihood (to you) for a time." | ""Ndipo sindikudziwa, mwina kuchedwetsa chilango chanu ndi mayeso akukuyesani ndikukusangalatsani ndi zokoma (za m'dziko) mpaka Idzakwane nthawi yoikidwayo." |
1.225869 | Or they may fear that they will find it difficult to live up to God's requirements after baptism. | Kapena angachite mantha kuti zidzawavuta kuchita zimene Mulungu amafuna akadzabatizidwa. |
1.225816 | "Why do you sit by yourself, and all the people stand before you from morning until evening?" | N'chifukwa chiyani wangokhala wekha kupereka ziweruzo ndipo anthu onse ali chiimire pamaso pako kuyambira m'mawa mpaka madzulo?" |
1.225771 | When she expressed this concern, Jesus plainly said to her: "You worship what you do not know." | Atamuuza vutoli, Yesu anamuuza momveka bwino kuti: "Inu mumalambira chimene simuchidziwa." |
1.225752 | shall not be accepted from them, and they shall have a painful punishment. | Ndiponso sadzawayeretsa (kumachimo awo); ndipo iwo adzapeza chilango chopweteka. |
1.225608 | it is a sound of a single-coil | monga mawu omveka, pamene khoma limodzi limaphimbidwa; |
1.225388 | And, indeed, I think he is a liar!" | Ndithu ine ndikumganizira kuti ndi mmodzi wa abodza." |
1.225353 | God answered the prayers of Solomon. | Mwachitsanzo, Solomo anachonderera Mulungu kuti aziyankha mapembedzero a olambira Ake. |
1.225239 | in God I have put my trust, I shall not be afraid. | mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha. |