Chichewa
stringlengths 10
500
| sentiment
stringclasses 2
values | __index_level_0__
int64 0
835k
|
---|---|---|
Kodi umboni umenewu ndi otani umene anthu awa akupereka kukutsutsa Iwe?"
|
Negative
| 0 |
Anthu atatu onsewa anasintha chonchi chifukwa choti ankafuna kutsanzira Khristu.
|
Negative
| 1 |
"Ndipo iye pamodzi ndi makamu ake ankhondo adadzitukumula pa dziko popanda chilungamo ndipo ankaganiza kuti iwo sadzabwelere kwa Ife.
|
Negative
| 2 |
njira yanji akuchotsedwa ku (choonadi)!
|
Positive
| 3 |
"Ndipo opani Moto umene wakonzedwa kwa (anthu) osakhulupirira.
|
Negative
| 4 |
"Tawafunsani nkhani ya mudzi umene udali m'mphepete mwa nyanja; (anthu am'mudziwo) pamene adali kuswa (lamulo la) tsiku la Sabata (lomwe adauzidwa kuti pa tsikuli asamachite usodzi wa nsomba, koma m'malo mwake azichita mapemphero okha).
|
Negative
| 5 |
Amapereka moyo ndikupereka imfa, Mbuye wanu ndi Mbuye wa makolo anu oyamba.
|
Positive
| 6 |
"Ndipo motero tidampatsa ulemelero Yûsuf m'dziko (la Iguputo); amakhala m'menemo paliponse pamene wafuna.
|
Positive
| 7 |
"Ndipo munthu (wokanira) amanena: "Kodi ndikadzafa nzoonadi kuti Ndidzatulutsidwa (m'manda) nkukhala wamoyo?"
|
Negative
| 8 |
Iye anayenda nane mwamtendere ndi molungama mtima, ndipo anabweza anthu ambiri mʼnjira zawo zauchimo.
|
Positive
| 9 |
N'zimene zinawasonkhezera kukwaniritsa zimene anachita."
|
Positive
| 10 |
Kodi Qur'an sinadzudzule ma Arabu achikunja chifukwa
|
Negative
| 11 |
Ngakhale kuti kukhalapo kwake monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu n'kosaoneka, umboni wake ukuoneka chifukwa cha kukwaniritsidwa kwa maulosi.
|
Negative
| 12 |
Ndipo A'adi adaonongedwa ndi chimphepo
|
Positive
| 13 |
Ndipo iye adaitana Mbuye wake kuti: "Awa ndithu ndi anthu oipa."
|
Negative
| 14 |
""Ndithu Allah ndiye Mbuye wanga ndi Mbuye wanunso; choncho mupembedzeni; imeneyi ndiyo njira yolunjika."
|
Positive
| 15 |
"Ndipo kachisanu (alumbire) kuti matembelero a Allah akhale pa iye ngati (iye) ali m'modzi mwa onama.
|
Negative
| 16 |
(Zikadzachitika zimenezi) mzimu Uliwonse udzadziwa zimene Wabweretsa (zabwino ndi zoipa).
|
Positive
| 17 |
Kuti tithawe kuchoka mnyanja yamoto, kulibe njira ina iliyonse koma kuti maina athu alembedwe mu Buku la Moyo.
|
Negative
| 18 |
ndipo amasiyira chuma chawo anthu ena.
|
Positive
| 19 |
"Ndipo ndithu tidasiya chizindikiro mmenemo choonekera kwa anthu anzeru.
|
Positive
| 20 |
Atumize Mzimu Wanu, ndipo iwo adzakhala analenga.
|
Positive
| 21 |
"Kodi saona momwe Allah ayambitsira zolengedwa, kenako nkuzibwerezanso?
|
Negative
| 22 |
"Koma amene waopa kuti adzaimitsidwa kwa Mbuye wake (pa nthawi ya chiweruziro), adzalandira minda iwiri (yaikulu yamtendere).
|
Negative
| 23 |
"Ndipo ngati utawafunsa: "Ndani adawalenga?"
|
Negative
| 24 |
"Ndithu Allah amakonda amene akumenya nkhondo pa njira Yake (yofalitsa chipembedzo Chake), ali pa mzere (umodzi) uku ali monga chomanga, chomangika mwamphamvu.
|
Positive
| 25 |
"M'menemo ndi momwe tikulongosolera mokwanira zivumbulutso kuti mwina iwo angabwelere (kwa Allah).
|
Positive
| 26 |
(Komanso) ndinasonkhanitsa anthu onse (amene ankakhala m'mizindayo) ndipo ndinawalamula kuti abwerere kumizinda yawo."
|
Positive
| 27 |
Ndipo iwo adzakhala ndi moyo m'dziko lawo, limene ndinapatsa mtumiki wanga Yakobo.
|
Positive
| 28 |
Koma amene angafune (zina) Kusiya zimenezi iwowo ndiwo Olumpha malire.
|
Positive
| 29 |
Ndithu m'zimenezo muli malingaliro kwa kapolo aliyense wotembenukira (kwa Allah).
|
Positive
| 30 |
""Ndithu ine ndikukuoperani chilango cha tsiku lalikulu."
|
Negative
| 31 |
Ndipo adzawalowetsa m'minda yomwe pansi pake pakuyenda mitsinje; adzakhala m'menemo muyaya.
|
Positive
| 32 |
" (Zikadzachitika zimenezi) mzimu uliwonse udzadziwa zimene wabweretsa (zabwino ndi zoipa).
|
Positive
| 33 |
Ndithudi, yemwe mudzamulowetse ku Moto ndiye kuti mwamuyalutsa, ndipo sipadzakhala athandizi kwa ochita zoipa."
|
Negative
| 34 |
"Ndipo angelo awiriwa anadza ku Sodomu madzulo, pamene Loti adakhala pachipata cha Sodomu.
|
Negative
| 35 |
Komanso tikulimbikitsidwa ndi mawu akuti: 'Omwe aopa Mulungu adzapeza bwino.'
|
Positive
| 36 |
"Kwa yemwe mwa inu akufuna kuyenda mu njira yoongoka.
|
Positive
| 37 |
Ndipo munthu adati kwa ena,
|
Positive
| 38 |
Ukadzatuluka udzakhala wokalamba komanso wekhawekha."
|
Negative
| 39 |
Qur'an inabvumbulutsidwa Mmwezi wa Ramadhan, choncho Allah anaupanga mwezi wa Ramadhan kukhala wabwino kuposa myezi yonse.
|
Positive
| 40 |
"Ndithu Ife tidawatumizira chimphepo champhamvu choulutsa miyala (ndi kuwagenda), kupatula akubanja la Luti; tidawapulumutsa (ku chilangocho) m'bandakucha,
|
Negative
| 41 |
Thangwe nsiku za wanthu wangu, zin'dzakhala ninga nsiku za muti, ndipo omwe ndawasankhulawo, wan'dzapfatsa na mabasa yakuphatidwa na manja yawo.'
|
Positive
| 42 |
Ndipo opani Allah, dziwani kuti Allah Ngwaukali polanga.
|
Negative
| 43 |
Ine sindili chilichonse koma mchenjezi ndi wouza anthu okhulupirira nkhani zabwino."
|
Positive
| 44 |
Kumwamba kapena kwa anthu?"
|
Positive
| 45 |
Ngati helo alidi malo ozunzirako anthu, m'pake kuopa.
|
Negative
| 46 |
"Kenako kudzanenedwa kwa amene adachita zoipa: "Lawani chilango chamuyaya!
|
Negative
| 47 |
"Ndipo Ayah Zathu zikawerengcdwa kwa iwo zolongosola chilichonse momveka, alibe mtsutso wina koma kunena kuti: "Tibweretsereni makolo Athu (aukitseni akhale ndi moyo) ngati inu muli owona!"
|
Positive
| 48 |
""Kupatula akapolo Anu omwe ali osankhidwa (oyeretsedwa) mwa iwo.
|
Positive
| 49 |
"Nena: "E inu amene mudapatsidwa buku! chifukwa chiyani mukuzikana zizindikiro za Allah pomwe Allah ndi Mboni wa zonse zimene mukuchita?"
|
Negative
| 50 |
Komabe, umboni wosatulutsa mawu wa zinthu zakumwamba ndi wamphamvu kwambiri.
|
Positive
| 51 |
Kotero kodi izo kutsatira kuti ife kuba, ku nyumba ya mbuye wanu, golide kapena siliva?
|
Negative
| 52 |
Ndithu taphunzitsidwa (mpaka tikudziwa) chiyankhulo cha mbalame, ndiponso tapatsidwa chilichonse; ndithu umenewu ndiubwino wopenyeka.
|
Positive
| 53 |
Yosefe atawaona, anazindikira kuti akuda nkhawa ndi zinazake ndipo anawafunsa kuti: "N'chifukwa chiyani nkhope zanu zili zachisoni lero?"
|
Negative
| 54 |
Ndipo ndithu lonjezo lanu ndiloona, ndipo Inu Ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse."
|
Positive
| 55 |
"Ndipo tidampulumutsa iye ndi anthu ake ku vuto lalikulu.
|
Positive
| 56 |
Ngati ndinu wachinyamata ndipo mwakumana ndi zimenezi, muyenera kuganizira za Mose.
|
Negative
| 57 |
Kodi sakuona kuti ilo (fano lawolo) silikuwalankhula ndiponso silikuwaongolera njira (yabwino?)
|
Negative
| 58 |
"Ndithudi, taona kutembenukatembenuka kwa nkhope yako (kuyang'ana) kumwamba.
|
Positive
| 59 |
Ambuye ali pafupi."
|
Positive
| 60 |
Choncho Mulungu anamulanga ndi matenda oopsa akhate.
|
Negative
| 61 |
Ndipo ndithu, lonjezo lanu ndiloona, ndipo inu ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse."
|
Positive
| 62 |
"Onse awa, (abwino ndi oipa), timawapatsa awa ndi awa mwazopatsa za Mbuye wako; ndipo zopatsa za Mbuye wako sizotsekerezedwa (kuti zisamfike kapolo Wake).
|
Positive
| 63 |
Chonchotu, atibweretsere chizizwa monga mmene adatumiziridwa (aneneri) oyamba."
|
Negative
| 64 |
Ameneyu ndiye mwamuwona kuti ndiye wofunika punishment?
|
Negative
| 65 |
Taonani,"Iye anati, "Moto ndi nkhuni.
|
Positive
| 66 |
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa masiku a njala.
|
Negative
| 67 |
Kodi angathe kukuthandizani kapena kudzithandiza okha?"
|
Negative
| 68 |
Mbuye wako wanena (kuti): 'Izi nzofewa kwa Ine; ndithu ndidakulenga kale pomwe iwe sudali kanthu."
|
Positive
| 69 |
"Kamuuzeni mawu ofewa mwina akalingalira (uthengawo) kapena akaopa.
|
Positive
| 70 |
"Ndipo (Nuh) adati: "Kwerani m'menemo mwadzina la Allah mkuyenda kwake ndi mkukocheza kwake.
|
Positive
| 71 |
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa Masiku a njala
|
Negative
| 72 |
Pamene muwerenga, kumbukirani ndi uthenga wa Mulungu kwa inu ngati munthu.
|
Positive
| 73 |
"Ndipo tidawagawa iwo m'mafuko khumi ndi awiri (osiyanasiyana) monga mitundu ikuluikulu.
|
Negative
| 74 |
mwanayo) adzamuyamwitsira (mkazi) wina,
|
Positive
| 75 |
"Ndipo mwa amene tidawalenga, alipo anthu oongolera (anzawo) ku choonadi.
|
Positive
| 76 |
Kapena angachite mantha kuti zidzawavuta kuchita zimene Mulungu amafuna akadzabatizidwa.
|
Negative
| 77 |
N'chifukwa chiyani wangokhala wekha kupereka ziweruzo ndipo anthu onse ali chiimire pamaso pako kuyambira m'mawa mpaka madzulo?"
|
Negative
| 78 |
Atamuuza vutoli, Yesu anamuuza momveka bwino kuti: "Inu mumalambira chimene simuchidziwa."
|
Positive
| 79 |
Ndiponso sadzawayeretsa (kumachimo awo); ndipo iwo adzapeza chilango chopweteka.
|
Negative
| 80 |
monga mawu omveka, pamene khoma limodzi limaphimbidwa;
|
Negative
| 81 |
Ndithu ine ndikumganizira kuti ndi mmodzi wa abodza."
|
Negative
| 82 |
Mwachitsanzo, Solomo anachonderera Mulungu kuti aziyankha mapembedzero a olambira Ake.
|
Positive
| 83 |
mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha.
|
Positive
| 84 |
Ndipo, ndithudi, ngati pali mwamuna mu aquarium iyi.
|
Negative
| 85 |
Iwo sayenera amafanana zovala zachimuna kapena zovala za osakhulupirira.
|
Negative
| 86 |
"Pamene m'bale wawo (Mneneri) Hûd adawafunsa kuti: "Kodi simuopa (Allah)?"
|
Positive
| 87 |
"Kufikira pamene adzatidzera (tsiku la Qiyâma, uku akulowetsedwa ku Moto).
|
Positive
| 88 |
Atate, ndipulumutseni Ine ku nthaŵi iyi."
|
Negative
| 89 |
"Mawa lino adzadziwa (tsiku lakuwatsikira chilango,) kuti ndiyani wabodza wodzitukumula (iwo kapena Swaleh).
|
Negative
| 90 |
"Nena: "Yendani pa dziko ndi kuona momwe Allah adayambitsira chilengedwe; kenako Allah adzaumba, kuumba kwina.
|
Positive
| 91 |
Chifukwa ndaona zonse zimene Labani wachita kwa inu.
|
Negative
| 92 |
Amphaka ngati dzina lawo limveka;
|
Positive
| 93 |
"Kotero alemekezeke Yemwe m'manja Mwake muli ulamuliro pa chinthu chilichonse; ndipo kwa Iye (ndiko) mudzabweerera nonse.
|
Positive
| 94 |
"Zimenezo nchifukwa chakuti iwo adakonda moyo wa dziko lapansi kwambiri kuposa wa pambuyo pa imfa; ndi kutinso Allah saongola anthu osakhulupirira.
|
Negative
| 95 |
M'nthaka muli zizindikiro kwa Otsimikiza, (Zosonyeza kuti Mulungu alipo).
|
Positive
| 96 |
ndipo zaka za moyo wako zidzakhala zochuluka.
|
Positive
| 97 |
Uchiteni mzinda uwu (wa Makka) kukhala wa mtendere; ndipo ndipatuleni ine ndi ana anga ku machitidwe opembedza mafano."
|
Positive
| 98 |
Zikomo...izo anali Old School.
|
Positive
| 99 |
Chichewa Sentiment Corpus
Dataset Description
This dataset contains sentiment-labeled text data in Chichewa for binary sentiment classification (Positive/Negative). Sentiments are extracted and processed from the English meanings of the sentences using DistilBERT for sentiment classification. The dataset is part of a larger collection of African language sentiment analysis resources.
Dataset Statistics
- Total samples: 834,916
- Positive sentiment: 450225 (53.9%)
- Negative sentiment: 384691 (46.1%)
Dataset Structure
Data Fields
- Text Column: Contains the original text in Chichewa
- sentiment: Sentiment label (Positive or Negative only)
Data Splits
This dataset contains a single split with all the processed data.
Data Processing
The sentiment labels were generated using:
- Model:
distilbert-base-uncased-finetuned-sst-2-english
- Processing: Batch processing with optimization for efficiency
- Deduplication: Duplicate entries were removed based on text content
- Filtering: Only Positive and Negative sentiments retained for binary classification
Usage
from datasets import load_dataset
# Load the dataset
dataset = load_dataset("michsethowusu/chichewa-sentiments-corpus")
# Access the data
print(dataset['train'][0])
# Check sentiment distribution
from collections import Counter
sentiments = [item['sentiment'] for item in dataset['train']]
print(Counter(sentiments))
Use Cases
This dataset is ideal for:
- Binary sentiment classification tasks
- Training sentiment analysis models for Chichewa
- Cross-lingual sentiment analysis research
- African language NLP model development
Citation
If you use this dataset in your research, please cite:
@dataset{chichewa_sentiments_corpus,
title={Chichewa Sentiment Corpus},
author={Mich-Seth Owusu},
year={2025},
url={https://huggingface.co/datasets/michsethowusu/chichewa-sentiments-corpus}
}
License
This dataset is released under the MIT License.
Contact
For questions or issues regarding this dataset, please open an issue on the dataset repository.
Dataset Creation
Date: 2025-07-02 Processing Pipeline: Automated sentiment analysis using HuggingFace Transformers Quality Control: Deduplication, batch processing optimizations, and binary sentiment filtering applied
- Downloads last month
- 11